Ndikhulupilira Bible (Official Video) — Area 47 Senior Youth Choir

Words & Music: Ndudirim Nwachukwu Accessed from: Tunefulness.scores Title: Oh yes, I believe ‪@tunefulness.scores‬ _________________________________________ Chichewa Lyrics: 1. Ndikhulupilira Bible, Ndukhulupilira Yesu, Kuti anafa pamtanda kufera 'ne. Ndikhulupirira Tate, Mwana ndi Mzimu Oyera, Ine, ine, ndikhulupira. Chorus Kuti anandiferane, Kuti ndikhale ndi moyo. Anafa, anafa, anafa kufera ine, Akufuna ndisiye tchimo, anafa pamtanda paja, Nagwazidwa Mbuye wanga. 2. Ndikhulupilira Yesu, Abweradi posachedwa, Kudzatenga onse kunka nawo mwamba. Kuti tikhale ndi moyo, Osatha mudziko ilo, Ine ine ndikhulupira.